Genesis 3:6

Genesis 3:6 CCL

Pamene mkaziyo anaona kuti mtengowo unali wabwino kudya ndi wokongola ndi kuti unali wopatsa nzeru, anatengako zipatso zake nadya. Zina anamupatsako mwamuna wake amene anali naye pomwepo ndipo naye anadyanso.

与Genesis 3:6相关的免费读经计划和灵修短文