YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Yoh. 2 的热门经文

1

Yoh. 2:11

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adaonetsa chizindikiro chake choyambachi m'mudzi wa Kana m'dera la Galileya. Pamenepo adaonetsa ulemerero wake, ndipo ophunzira ake adamkhulupirira.

对照

探索 Yoh. 2:11

2

Yoh. 2:4

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adayankha kuti, “Mai, kodi mukuti nditani? Nthaŵi yangatu siinafike.”

对照

探索 Yoh. 2:4

3

Yoh. 2:7-8

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Yesu adauza anyamata aja kuti, “Dzazani mbiyazi ndi madzi.” Ndipo adazidzaza mpaka m'milomo. Pambuyo pake adaŵauza kuti, “Tsopano tungani, kaperekeni kwa mkulu wa phwando,” Iwowo adakaperekadi.

对照

探索 Yoh. 2:7-8

4

Yoh. 2:19

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Yesu adaŵayankha kuti, “Gwetsani nyumba ya Mulungu ino, Ine ndidzaimanganso masiku atatu.”

对照

探索 Yoh. 2:19

5

Yoh. 2:15-16

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Apo Yesu adapanga mkwapulo wazingwe nayamba kuŵatulutsira onse kunja, pamodzi ndi nkhosa ndi ng'ombe zao zomwe. Adagubudula matebulo a osinthitsa ndalama aja, naŵamwazira ndalama zao. Ndipo adalamula ogulitsa nkhunda aja kuti, “Izi zitulutseni muno. Nyumba ya Atate anga musaisandutse nyumba yochitiramo malonda.”

对照

探索 Yoh. 2:15-16

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频