1
Gen. 2:24
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.
对照
探索 Gen. 2:24
2
Gen. 2:18
Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”
探索 Gen. 2:18
3
Gen. 2:7
Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.
探索 Gen. 2:7
4
Gen. 2:23
Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”
探索 Gen. 2:23
5
Gen. 2:3
Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.
探索 Gen. 2:3
6
Gen. 2:25
Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.
探索 Gen. 2:25
YouVersion 使用 cookie 来个性化你的体验。使用我们的网站,即表示你同意我们根据我们的隐私政策来使用 cookie。
主页
圣经
计划
视频