YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

LUKA 23 的热门经文

1

LUKA 23:34

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu ananena, Atate, muwakhululukire iwo, pakuti sadziwa chimene achita. Ndipo anagawana zovala zake, poyesa maere.

对照

探索 LUKA 23:34

2

LUKA 23:43

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine m'Paradaiso.

对照

探索 LUKA 23:43

3

LUKA 23:42

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ananena, Yesu, ndikumbukireni m'mene mulowa Ufumu wanu.

对照

探索 LUKA 23:42

4

LUKA 23:46

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene Yesu anafuula ndi mau akulu, anati, Atate, m'manja mwanu ndipereka mzimu wanga. Ndipo pakutero anapereka mzimu wake.

对照

探索 LUKA 23:46

5

LUKA 23:33

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene anafika kumalo dzina lake Bade, anampachika Iye pamtanda pomwepo, ndi ochita zoipa omwe, mmodzi kudzanja lamanja ndi wina kulamanzere.

对照

探索 LUKA 23:33

6

LUKA 23:44-45

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ora lake pamenepo linali ngati lachisanu ndi chimodzi. Ndipo panali mdima pa dziko lonse kufikira ora lachisanu ndi chinai, ndipo dzuwa linada. Ndipo nsalu yotchinga ya m'Kachisi inang'ambika pakati.

对照

探索 LUKA 23:44-45

7

LUKA 23:47

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene kenturiyo anaona chinachitikacho, analemekeza Mulungu, nanena, Zoonadi munthu uyu anali wolungama.

对照

探索 LUKA 23:47

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频