YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

LUKA 16 的热门经文

1

LUKA 16:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Iye amene akhulupirika m'chaching'onong'ono alinso wokhulupirika m'chachikulu; ndipo iye amene ali wosalungama m'chachikulu.

对照

探索 LUKA 16:10

2

LUKA 16:13

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe mnyamata wa m'nyumba akhoza kukhala kapolo wa ambuye awiri; pakuti kapena adzamuda wina, nadzakonda winayo; kapena adzatsata wina, nadzapeputsa winayo. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Chuma.

对照

探索 LUKA 16:13

3

LUKA 16:11-12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake ngati simunakhala okhulupirika m'chuma cha chosalungama, adzakhulupirira inu ndani ndi chuma choona? Ndipo ngati simunakhala okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni?

对照

探索 LUKA 16:11-12

4

LUKA 16:31

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.

对照

探索 LUKA 16:31

5

LUKA 16:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yense wakusudzula mkazi wake, nakwatira wina, achita chigololo; ndipo iye amene akwatira wosudzulidwayo, achita chigololo.

对照

探索 LUKA 16:18

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频