YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

YOHANE 2 的热门经文

1

YOHANE 2:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita m'Kana wa m'Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

对照

探索 YOHANE 2:11

2

YOHANE 2:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

对照

探索 YOHANE 2:4

3

YOHANE 2:7-8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

对照

探索 YOHANE 2:7-8

4

YOHANE 2:19

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

对照

探索 YOHANE 2:19

5

YOHANE 2:15-16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse m'Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

对照

探索 YOHANE 2:15-16

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频