YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 45 的热门经文

1

GENESIS 45:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tsopano musapwetekwe mtima, musadzikwiyira inu nokha, kuti munandigulitsa ine kuno, pakuti Mulungu ananditumiza ine patsogolo panu kuti ndisunge moyo.

对照

探索 GENESIS 45:5

2

GENESIS 45:8

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo tsopano sindinu amene munanditumiza ine ndifike kuno, koma Mulungu, ndipo anandiyesa ine atate wa Farao, ndi mwini banja lake lonse, ndi wolamulira dziko lonse la Ejipito.

对照

探索 GENESIS 45:8

3

GENESIS 45:7

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Mulungu anatumiza ine patsogolo panu kuti ndikhazike inu mutsale m'dziko lapansi, ndi kusunga inu amoyo ndi chipulumutso chachikulu.

对照

探索 GENESIS 45:7

4

GENESIS 45:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anati kwa abale ake, Muyandikiretu kwa ine; nayandikira. Ndipo iye anati, Ine ndine Yosefe mbale wanu, ine ndemwe munandigulitsa ndilowe m'Ejipito.

对照

探索 GENESIS 45:4

5

GENESIS 45:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Zaka ziwirizi muli njala m'dziko muno; ndipo zatsala zaka zisanu, zopanda kulima kapena kusenga.

对照

探索 GENESIS 45:6

6

GENESIS 45:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anati kwa abale ake, Ine ndine Yosefe; kodi akali ndi moyo atate wanga? Ndipo abale ake sanakhoze kumyankha iye; pakuti anavutidwa pakumuona iye.

对照

探索 GENESIS 45:3

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频