1
GENESIS 29:20
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Yakobo anamtumikira zaka zisanu ndi ziwiri chifukwa cha Rakele; koma zidamuonekera iye ngati masiku owerengeka chifukwa cha chikondi chimene anamkonda iye nacho.
对照
探索 GENESIS 29:20
2
GENESIS 29:31
Pamene Yehova anaona kuti anamuda Leya, anatsegula m'mimba mwake; koma Rakele anali wouma.
探索 GENESIS 29:31
主页
圣经
计划
视频