YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 26 的热门经文

1

GENESIS 26:3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

khala mlendo m'dziko muno, ndipo Ine ndidzakhala ndi iwe, ndipo ndidzadalitsa iwe chifukwa kuti ndidzakupatsa iwe ndi mbeu zako maiko onse awa, ndipo ndidzalimbikitsa chilumbiriro ndinachilumbirira kwa Abrahamu atate wako

对照

探索 GENESIS 26:3

2

GENESIS 26:4-5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo ndidzachulukitsa mbeu zako monga nyenyezi za kumwamba, ndipo ndidzapatsa mbeu zako maiko onsewa; m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsidwa; chifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga chilangizo changa, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga.

对照

探索 GENESIS 26:4-5

3

GENESIS 26:22

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anachoka kumeneko nakumba chitsime china; koma sanakangane nacho chimenecho; ndipo anatcha dzina lake Rehoboti; ndipo anati, Chifukwa kuti tsopano Yehova anatipatsa ife malo, ndipo tidzabalana m'dziko muno.

对照

探索 GENESIS 26:22

4

GENESIS 26:2

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anamuonekera iye nati, Usatsikire ku Ejipito, khala m'dziko m'mene ndidzakuuza iwe

对照

探索 GENESIS 26:2

5

GENESIS 26:25

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anamanga kumeneko guwa la nsembe, naitana dzina la Yehova, namanga hema wake kumeneko: ndi pamenepo anyamata a Isaki anakumba chitsime.

对照

探索 GENESIS 26:25

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频