YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 21 的热门经文

1

GENESIS 21:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yehova anayang'anira Sara monga momwe anati, ndipo Yehova anamchitira iye monga ananena.

对照

探索 GENESIS 21:1

2

GENESIS 21:17-18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Mulungu anamva mau a mnyamatayo, ndi mthenga wa Mulungu anamuitana Hagara, ndi mau odzera kumwamba, nati kwa iye, Watani Hagara? Usaope; chifukwa Mulungu anamva mau a mnyamata kumene ali. Tauka, nuukitse mnyamatayo, ndi kumgwira m'dzanja lako; chifukwa ndidzamuyesa iye mtundu waukulu.

对照

探索 GENESIS 21:17-18

3

GENESIS 21:2

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Sara anatenga pakati, nambalira Abrahamu m'ukalamba wake mwana wamwamuna, nthawi yomweyo Mulungu anamuuza iye.

对照

探索 GENESIS 21:2

4

GENESIS 21:6

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Sara anati, Mulungu anandisekeretsa ine; onse akumva adzasekera pamodzi ndi ine.

对照

探索 GENESIS 21:6

5

GENESIS 21:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Mulungu anati kwa Abrahamu, Usaipidwe nao, chifukwa cha mnyamatayo, ndi chifukwa cha mdzakazi wako; momwe monse akunenera iwe Sara umvere iwe mau ake; chifukwa kuti mwa Isaki zidzaitanidwa mbeu zako.

对照

探索 GENESIS 21:12

6

GENESIS 21:13

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mwana wamwamuna wa mdzakazi uyo ndidzayesa mtundu, chifukwa iye ndiye mbeu yako.

对照

探索 GENESIS 21:13

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频