YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

GENESIS 16 的热门经文

1

GENESIS 16:13

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anatcha dzina la Yehova amene ananena naye, Ndinu Mulungu wakundiona ine; pakuti anati, Kodi kunonso ndayang'ana pambuyo pake pa Iye amene wakundiona ine?

对照

探索 GENESIS 16:13

2

GENESIS 16:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mthenga wa Yehova anati kwa iye, Taona, uli ndi pakati, ndipo udzabala mwana wamwamuna; nudzamutcha dzina lake Ismaele; chifukwa Yehova anamva kusauka kwako.

对照

探索 GENESIS 16:11

3

GENESIS 16:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo iye adzakhala munthu wa m'thengo; ndipo dzanja lake lidzakhala lotsutsana ndi anthu onse, ndi manja a anthu onse adzakhala otsutsana naye: ndipo iye adzakhala pamaso pa abale ake onse.

对照

探索 GENESIS 16:12

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频