YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Yohane 5 的热门经文

1

Yohane 5:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene amamva mawu anga ndi kukhulupirira Iye amene ananditumiza Ine, ali ndi moyo wosatha ndipo sadzaweruzidwa. Iye wachoka mu imfa ndipo walowa mʼmoyo.

对照

探索 Yohane 5:24

2

Yohane 5:6

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu atamuona ali chigonere, nadziwa kuti anakhala chotero kwa nthawi yayitali, anamufunsa iye kuti, “Kodi ukufuna kuchira?”

对照

探索 Yohane 5:6

3

Yohane 5:39-40

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. Koma inu mukukana kubwera kwa Ine kuti mukhale ndi moyo.

对照

探索 Yohane 5:39-40

4

Yohane 5:8-9

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yesu anati kwa iye, “Imirira! Nyamula mphasa yako yamba kuyenda.” Nthawi yomweyo munthuyo anachiritsidwa. Iye ananyamula mphasa yake nayamba kuyenda. Tsiku limene izi zinachitika linali la Sabata.

对照

探索 Yohane 5:8-9

5

Yohane 5:19

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anawapatsa yankho ili: “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Mwana sangathe kuchita kanthu pa Iye yekha. Iye amachita zokhazo zimene amaona Atate ake akuchita, chifukwa chilichonse chimene Atate amachita Mwana amachitanso.

对照

探索 Yohane 5:19

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频