YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Yohane 2 的热门经文

1

Yohane 2:11

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ichi chinali chizindikiro chodabwitsa choyamba chimene Yesu anachita ku Kana wa ku Galileya. Potero Iye anawulula ulemerero wake, ndipo ophunzira ake anamukhulupirira Iye.

对照

探索 Yohane 2:11

2

Yohane 2:4

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anayankha kuti, “Amayi, chifukwa chiyani mukundiwuza Ine? Nthawi yanga sinakwane.”

对照

探索 Yohane 2:4

3

Yohane 2:7-8

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anati kwa antchitowo, “Dzazani madzi mʼmitsukoyi,” ndipo iwo anadzaza ndendende. Ndipo Iye anatinso kwa iwo, “Tsopano tungani ndipo kaperekeni kwa mkulu waphwando.” Iwo anachita momwemo.

对照

探索 Yohane 2:7-8

4

Yohane 2:19

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yesu anawayankha kuti, “Gwetsani Nyumba ya Mulunguyi ndipo Ine ndidzayimanganso mʼmasiku atatu.”

对照

探索 Yohane 2:19

5

Yohane 2:15-16

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Chifukwa cha zimenezi Iye anapanga chikwapu cha zingwe ndipo anatulutsa onse mʼbwalo la Nyumbayo, pamodzi ndi nkhosa ndi ngʼombe; Iye anamwaza ndalama zawo ndi kugudubuza matebulo. Kwa amene amagulitsa nkhunda, Iye anati, “Tulutsani izi muno! Osasandutsa Nyumba ya Atate anga msika!”

对照

探索 Yohane 2:15-16

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频