YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Genesis 7 的热门经文

1

Genesis 7:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova anati kwa Nowa, “Lowa mu chombo iwe ndi banja lako lonse, chifukwa ndaona kuti ndiwe wolungama mu mʼbado uwu.

对照

探索 Genesis 7:1

2

Genesis 7:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Madziwo anadzaza dziko lonse lapansi kwa masiku 150.

对照

探索 Genesis 7:24

3

Genesis 7:11

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Pa tsiku la 17 la mwezi wachiwiri, Nowa ali ndi zaka 600, akasupe onse akuya kwambiri anasefuka ndiponso zitseko za madzi akumwamba zinatsekuka.

对照

探索 Genesis 7:11

4

Genesis 7:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Chamoyo chilichonse pa dziko lapansi chinawonongedwa, kuyambira munthu, nyama, zokwawa ndi mbalame. Nowa yekha ndiye anatsala pamodzi ndi onse amene anali naye.

对照

探索 Genesis 7:23

5

Genesis 7:12

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo mvula inagwa pa dziko lapansi masiku makumi anayi usana ndi usiku.

对照

探索 Genesis 7:12

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频