YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Genesis 4 的热门经文

1

Genesis 4:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ukanachita zabwino sindikanakulandira kodi? Koma tsopano wachita zoyipa ndipo tchimo likukudikira pa khomo pako, likufuna kukugwira; koma iwe uyenera kugonjetsa tchimolo.”

对照

探索 Genesis 4:7

2

Genesis 4:26

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Seti naye anali ndi mwana wa mwamuna, ndipo anamutcha Enosi. Pa nthawi imeneyi anthu anayamba kupemphera mʼdzina la Yehova.

对照

探索 Genesis 4:26

3

Genesis 4:9

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova anamufunsa Kaini kuti, “Ali kuti mʼbale wako Abele?” Iye anayankha kuti, “Sindikudziwa. Kodi ine ndine wosunga mʼbale wanga?”

对照

探索 Genesis 4:9

4

Genesis 4:10

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yehova anati, “Kodi wachita chiyani? Tamvera! Magazi a mʼbale wako akulirira kwa Ine kuchokera mʼnthaka.

对照

探索 Genesis 4:10

5

Genesis 4:15

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Koma Yehova anamuwuza kuti, “Sizidzatero ayi; aliyense amene adzaphe Kaini adzalangidwa ndi kulipiritsidwa kasanu ndi kawiri.” Pamenepo Yehova anayika chizindikiro pa Kaini kuti aliyense womupeza asamuphe.

对照

探索 Genesis 4:15

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频