YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Genesis 2 的热门经文

1

Genesis 2:24

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi.

对照

探索 Genesis 2:24

2

Genesis 2:18

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Yehova Mulungu anati, “Sibwino kuti munthu akhale yekha. Ndidzamupangira mnzake womuthandiza.”

对照

探索 Genesis 2:18

3

Genesis 2:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.

对照

探索 Genesis 2:7

4

Genesis 2:23

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Munthu uja anati, “Uyu ndiye fupa lochokera ku mafupa anga ndi mnofu wochokera ku mnofu wanga; adzatchedwa ‘mkazi,’ popeza wachokera mwa mwamuna.”

对照

探索 Genesis 2:23

5

Genesis 2:3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ndipo Mulungu anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri nalipatula, chifukwa pa tsiku limeneli Iye anapumula ku ntchito yonse yolenga imene anayigwira.

对照

探索 Genesis 2:3

6

Genesis 2:25

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.

对照

探索 Genesis 2:25

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频