YouVersion 标志
圣经计划视频
获取软件
选择语言
搜索图标

Genesis 12 的热门经文

1

Genesis 12:2-3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Ndidzakusandutsa kholo la mtundu waukulu wa anthu ndipo ndidzakudalitsa; ndi kukusandutsa wotchuka kotero kuti udzakhala dalitso kwa anthu ambiri. Ndidzadalitsa amene adzadalitsa iwe, ndi kutemberera amene adzatemberera iwe; ndipo mafuko onse a pa dziko lapansi adzadalitsika kudzera mwa iwe.”

对照

探索 Genesis 12:2-3

2

Genesis 12:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Tsiku lina Yehova anamuwuza Abramu kuti, “Tuluka mʼdziko lako. Siya abale ako ndi banja la abambo ako ndipo pita ku dziko limene ndidzakusonyeza.

对照

探索 Genesis 12:1

3

Genesis 12:4

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Choncho Abramu ananyamuka monga momwe Yehova anamuwuzira, napita pamodzi ndi Loti. Pamene Abramu amachoka ku Harani nʼkuti ali ndi zaka 75.

对照

探索 Genesis 12:4

4

Genesis 12:7

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Yehova anadza kwa Abramu nati, “Kwa zidzukulu zako ndidzapereka dziko limeneli.” Choncho Abramu anamangira Yehova amene anadza kwa iye, guwa lansembe.

对照

探索 Genesis 12:7

上一章
下一章
YouVersion

我们要鼓励、挑战你每天亲近上帝。

事工

关于我们

就职机会

义工

博客

新闻区

有用链接

帮助

捐赠

圣经译本

音频圣经

译本语言

今日经文


此数字事工属于

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

隐私政策使用条款
漏洞披露方案
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

主页

圣经

计划

视频