Maluko 9:28-29

Maluko 9:28-29 NTNYBL2025

Ndiipo, Yesu yapo wadalowa mnyumba, oyaluzidwa wake adamfunjha paokha, “Ndande yanji ife sitidakhoze kumchocha chiwanda chijha?” Yesu wadaakambila, “Chiwanda ngati ichi sichikoza kuchoka, ingakhale kwa kupembhelape.”

Àwọn Fídíò tó Jẹmọ́ ọ