1
Maluko 7:21-23
Nyanja
NTNYBL2025
Pakuti kuchokela mmitima ya wandhu, yachoka maganizo yoipa ni chigololo ni unghungu ni kupha, uhule ni khumbilo lo funa chuma chambili ni voipa ni unami ni kukafula ni khumbilo lofuna chigololo ni mbwinya ni usabwabwa. Voipa vimenevo vichoka mkati mwa wandhu, navo vimchita mundhu siwadavomelezeka kumlambila Mnungu.”
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Maluko 7:21-23
2
Maluko 7:15
Palibe chindhu chilowa mkati mwa mundhu kuchokela kubwalo icho chikhoza kumchita siwadavomelezeka kwa kumlambila Mnungu. Nambho icho chichoka mkati mwa mundhu ndeicho chimchita mundhu siwadavomelezeka kwa kumlambila Mnungu.
Ṣàwárí Maluko 7:15
3
Maluko 7:6
Yesu wadaayangha, “Agunghuli anyiimwe, mlosi Isaya wadakuloselani bwino anyiimwe, yapo wadalemba, ‘Mnungu wakamba, wandhu anyiawa anilimekeza kwa milomo yaope, nambho mitima yao, ilikutali niine.
Ṣàwárí Maluko 7:6
4
Maluko 7:7
Ni kunilambila kwawo sikufunika, pakuti ayaluza mayaluzo ya wandhupe ngati mayaluzo ya Mnungu.’”
Ṣàwárí Maluko 7:7
5
Maluko 7:8
“Anyiimwe muyasiya malamulo ya Mnungu ni kuchata chikhalidwe cha wandhu.”
Ṣàwárí Maluko 7:8
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò