1
Maluko 16:15
Nyanja
NTNYBL2025
Chimwecho wadaakambila, “Pitani kujhiko lonjhe la panjhi, mkalalikile wandhu wonjhe Uthenga Wabwino.
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Maluko 16:15
2
Maluko 16:17-18
Vizindikilo ivi sivikhale pamojhi ni anyiiwo siakhulupilile. Satumile mbhavu za jhina langa kuchocha viwanda ni kukamba kwa mkambo wina. Akagwila njoka kapina kumwa chalichonjhe chili ni sumu sichawenga. Siwaikile manja wandhu wodwala, nawo saalame.”
Ṣàwárí Maluko 16:17-18
3
Maluko 16:16
Mundhu waliyonjhe uyo wakhulupilila ni kubatizidwa, siwaomboledwe, nambho mundhu uyo wakana kukhulupilila siwalamulidwe.
Ṣàwárí Maluko 16:16
4
Maluko 16:20
Ndiipo oyaluzidwa wajha adapita kummalo yonjhe kwa lalikila wandhu Uthenga wa Bwino. Ambuye Yesu adachita njhito pamojhi ni anyiiwo ni kuchimikiza uthenga umenewo kwa vizindikilo ivo vidalingana Uthenga umenewo.
Ṣàwárí Maluko 16:20
5
Maluko 16:6
Mnyamata mmeneyo wadaakambila, “Simdajhujhumuka. Mumfunafuna Yesu wa ku Nazaleti uyo wadapachikidwa pamtanda. Wahyuka, balibepo pano. Penyani pamalo yapo adamgoneka.
Ṣàwárí Maluko 16:6
6
Maluko 16:4-5
Yapo adawandikila kufika adapenya, adaona mwala ujha wasendezedwa patali ni khomo la chiliza. Chimwecho adalowa pachiliza, adamuona mnyamata uyo wadavala viwalo voyela, wakhala bendeka la kwene la chijha chiliza, anyiiwo adajhujhumuka kupunda.
Ṣàwárí Maluko 16:4-5
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò