1
Maluko 10:45
Nyanja
NTNYBL2025
Ata, ine Mwana wa Mundhu sinidajhe kutumikilidwa, nambho kutumukila, ni kuchocha umoyo wanga kwa kwaombola wandhu ambili.”
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Maluko 10:45
2
Maluko 10:27
Yesu wadaapenyechecha ni kwaakambila, “Kwa mundhu siikhozekana, nambho kwa Mnungu ikhozekana, pakuti kila kandhu kwa Mnungu chikhozekana.”
Ṣàwárí Maluko 10:27
3
Maluko 10:52
Yesu wadamkambila, “Pita, kukhulupilila kwako kwakulamicha.” Pampajha, yujha sapenya wadakhoza kupenya, ndiipo wadamchata Yesu mnjila.
Ṣàwárí Maluko 10:52
4
Maluko 10:9
Chimwecho, icho wachilunjanicha Mnungu, mundhu siwadachisiyanicha.”
Ṣàwárí Maluko 10:9
5
Maluko 10:21
Yesu wadampenya ni wadamkonda, ni wadamkambila, “Wachepekeledwa ni chindhu chimojhi, pita ukaguliche kila chindhu ulinacho, ni ndalama izo siupate waapache wosauka, niiwe siukhale ni wopata kumwamba, ndiipo majha unichate.”
Ṣàwárí Maluko 10:21
6
Maluko 10:51
Yesu wadamfunjha, “Ufuna nikuchitile chiyani?” Sapenya yujha wadamuyangha, “Oyaluza, nipemhba nipenye.”
Ṣàwárí Maluko 10:51
7
Maluko 10:43
Nambho kwa anyiimwe siidakhala chimwecho, mundhu waliyonjhe uyo wafuna wakhale wamkulu, ifunika wakhale mbowa wa wonjhe.
Ṣàwárí Maluko 10:43
8
Maluko 10:15
Zenedi nikukambilani, mundhu waliyonjhe uyo siwaulandila Ufumu wa Mnungu ngati wana wang'onoang'ono umo aulandilila, siwalowelatu muufumu wa Mnungu.”
Ṣàwárí Maluko 10:15
9
Maluko 10:31
Nambho, yawo achogolela siakhale kumbuyo, ni akumbuyo siachogolele.”
Ṣàwárí Maluko 10:31
10
Maluko 10:6-8
Nambho, kuyambila kuumbidwa kwa jhiko, Mnungu wadaumba wamuna ni wamkazi. Chimwecho, wamuna siwasiye atate wake ni amake ni kulunjana ni mkazake, ni anyiiwo awili sakhale thupi limojhi. Chipano anyiiwo osati awilinjho, nambho ni thupi limojhi.
Ṣàwárí Maluko 10:6-8
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò