1
Matayo 25:40
Nyanja
NTNYBL2025
Mfumu siwaayanghe, ‘Zene nikukambilani, umo mwamchitila mmojhi wa anyiyawa abale wanga yawo sajhikoza, mwanichitila ine!’”
Ṣe Àfiwé
Ṣàwárí Matayo 25:40
2
Matayo 25:21
Mkulu wake wadamkambila, ‘Wachita bwino, iwe ni mbowa wabwino ni ukhulupilika. Pakuti udakhulupilika kwa vindhu vochepa, chipano sinikupache vindhu va vikulu, majha ukondwele pamojhi ni mkulu wako!’
Ṣàwárí Matayo 25:21
3
Matayo 25:29
Pakuti kila uyo wachitila njhito icho nampacha sinimchuluchile vina nayo siwakhale navo vambili. Nambho mundhu waliyonjhe uyo siwachitila njhito icho nimpacha, ata chaching'ono walinacho siwalandidwe.
Ṣàwárí Matayo 25:29
4
Matayo 25:13
Ndiipo Yesu wadamalizila kukamba, “Mjhipenyelele pakuti simujhiwa siku kapina saa.”
Ṣàwárí Matayo 25:13
5
Matayo 25:35
Nidali ni njala mdanipacha chakudya, ni nidali nilujho mdanipacha majhi ya kumwa, ni nidali mlendo mdanilandila mnyumba zanu.
Ṣàwárí Matayo 25:35
6
Matayo 25:23
Mkulu wake wadakamba, ‘Wachita bwino, iwe ni mbowa wabwino ni okhulupilika. Pakuti udali wokhulupilika kwa vindhu vochepa, sinikuike uimilile vindhu va vikulu, majha ukondwele pamojhi ni mkulu wako!’
Ṣàwárí Matayo 25:23
7
Matayo 25:36
Nidalibe njhalu mdaniveka, nidali odwala mdanidwaza ni nidali mndende mdaniyendela.’
Ṣàwárí Matayo 25:36
Ilé
Bíbélì
Àwon ètò
Àwon Fídíò