Uphawu lweYouVersion
IBhayibhileIzicwangcisoIividiyo
Fumana i-app
Isikhethi Solwimi
Khetha Uphawu

Iivesi zeBhayibhile ezithandwayo ezisuka GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Thelekisa

Phonononga GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Thelekisa

Phonononga GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Thelekisa

Phonononga GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Thelekisa

Phonononga GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Thelekisa

Phonononga GENESIS 7:12

Isahluko esidlulileyo
Isahluko Esilandelayo
I-YouVersion

Inkuthazo nomceli mngeni wokufuna usondelelwano noThixo, yonke imihla.

Inkonzo

Malunga

Imisebenzi

Volontiya

Ibhlogi

Cinezela

Amakhonco aluncedo

Uncedo

Nikela

Iinguqulelo zeBhayibhile

IiBhayibhile ezirekhodiweyo

Iilwimi zeBhayibhile

Ivesi yoLusuku


Inkonzo edijithali ka

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Umgaqo-Nkqubo WezabucalaImigaqo
Isibhengezo zokubasemngciphekweni
uFacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Ekuqaleni

IBhayibhile

Izicwangciso

Iividiyo