YouVersion Logo
بائبلمطالعاتی منصوبہVideos
اپلی کیشن حاصل کریں
زبان کا انتخاب کنندہ
تلاش

Eksodo 23 سے مشہور بائبلی آیات

1

Eksodo 23:25-26

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Muzipembedza Yehova Mulungu wanu ndipo adzakudalitsani ndi chakudya ndi madzi ndiponso ndidzachotsa nthenda pakati panu. Palibe mkazi amene adzapite padera kapena kukhala wosabereka mʼdziko mwanu. Ndidzakupatsani moyo wautali.

موازنہ

تلاش Eksodo 23:25-26

2

Eksodo 23:20

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Taona Ine ndikutuma mngelo wanga patsogolo panu kuti akutetezeni mʼnjiramo ndi kukakufikitsani ku malo amene ndakonza.

موازنہ

تلاش Eksodo 23:20

3

Eksodo 23:22

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

Ngati mudzamvera iyeyu ndi kuchita zonse zimene Ine ndikunena, Ine ndidzakhala mdani wa adani anu ndipo ndidzatsutsana ndi onse otsutsana nanu.

موازنہ

تلاش Eksodo 23:22

4

Eksodo 23:2-3

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Usatsate gulu la anthu ndi kuchita choyipa. Pamene ukupereka umboni mʼbwalo lamilandu, usakhotetse mlandu chifukwa chofuna kukondweretsa anthu ambiri. Ndipo poweruza mlandu wa munthu wosauka usamukondere.

موازنہ

تلاش Eksodo 23:2-3

5

Eksodo 23:1

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

CCL

“Usafalitse mbiri yabodza. Usathandize munthu wolakwa pomuchitira umboni wonama.

موازنہ

تلاش Eksodo 23:1

پچھلا باب
اگلا باب
YouVersion

آپ کو ہر روز خدا کے ساتھ قربت حاصل کرنے کی ترغیب دینا اور چیلنج کرنا۔.

خدمت

بارے میں

آسامیاں

رضاکار

Blog

Press

Useful Links

مدد

ہدیہ دیں

بائبل ورژن

Audio Bibles

بائبل کی زبانیں

آج کی آیت


کی ایک ڈیجیٹل خدمت

Life.Church
اردو

©2026 Life.Church / YouVersion

Privacy Policyشرائط
حساس کا انکشاف کرنے والا عمل
FacebookTwitterInstagramیوٹیوبپنٹیرسٹ