Mufananidzo weYouVersion
Mucherechedzo Wekutsvaka

Mateyu 14:16-17

Mateyu 14:16-17 CCL

Yesu anawayankha kuti, “Sikofunika kuti azipita. Inuyo muwapatse kanthu kuti adye.” Iwo anayankha kuti, “Tili ndi malofu asanu okha a buledi ndi nsomba ziwiri.”