1
EKSODO 14:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Yehova adzakugwirirani nkhondo, ndipo inu mudzakhala chete.
Compare
EKSODO 14:14ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
2
EKSODO 14:13
Ndipo Mose ananena ndi anthu, Musaope, chilimikani, ndipo penyani chipulumutso cha Yehova, chimene adzakuchitirani lero; pakuti Aejipito mwawaona lerowa, simudzawaonanso konse.
EKSODO 14:13ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
3
EKSODO 14:16
Ndipo iwe nyamula ndodo yako, nutambasulire dzanja lako kunyanja, nuigawe, kuti ana a Israele alowe pakati pa nyanja pouma.
EKSODO 14:16ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
4
EKSODO 14:31
Ndipo Israele anaiona ntchito yaikulu imene Yehova anachitira Aejipito, ndipo anthuwo anaopa Yehova; nakhulupirira Yehova ndi mtumiki wake Mose.
EKSODO 14:31ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
Home
ਬਾਈਬਲ
Plans
ਵੀਡੀਓ