1
EKSODO 13:21-22
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo Yehova anawatsogolera usana ndi mtambo njo kuwatsogolera m'njira; ndi usiku ndi moto njo, wakuwawalitsira; kuti ayende usana ndi usiku; sanachotse mtambo usana, kapena mtambo wamoto usiku, pamaso pa anthu.
Compare
EKSODO 13:21-22ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
2
EKSODO 13:17
Ndipo kunakhala pamene Farao adalola anthu amuke, Mulungu sanawatsogolere njira ya dziko la Afilisti, ndiyo yaifupi; pakuti Mulungu anati, Angadodome anthuwo pakuona nkhondo ndi kubwerera m'mbuyo kunka ku Ejipito.
EKSODO 13:17ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
3
EKSODO 13:18
Koma Mulungu anawazungulitsa anthuwo, ku njira ya kuchipululu ya Nyanja Yofiira; ndipo ana a Israele anakwera kuchokera m'dziko la Ejipito okonzeka.
EKSODO 13:18ਪੜਚੋਲ ਕਰੋ
Home
ਬਾਈਬਲ
Plans
ਵੀਡੀਓ