YouVersion logo
BijbelLeesplannenVideo's
Download de app
Taalkiezer
Zoek icoon

Populaire Bijbelverzen uit GENESIS 13

1

GENESIS 13:15

Buku Lopatulika

BLP-2018

chifukwa kuti dziko lonse limene ulinkuona, ndidzakupatsa iwe ndi mbeu yako nthawi yonse.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 13:15

2

GENESIS 13:14

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, atalekana naye Loti, Tukulatu maso ako, nuyang'anire kuyambira kumene uliko, kumpoto, ndi kumwera, ndi kum'mawa, ndi kumadzulo

Vergelijk

Ontdek GENESIS 13:14

3

GENESIS 13:16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo ndidzayesa mbeu yako monga fumbi lapansi: chotere kuti ngati munthu angathe kuwerenga fumbi lapansi, chomwechonso mbeu yako idzawerengedwa.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 13:16

4

GENESIS 13:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Abramu anati kwa Loti, Tisachite ndeu, ine ndi iwe, abusa anga ndi abusa ako: chifukwa kuti ife ndife abale.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 13:8

5

GENESIS 13:18

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Abramu anasuntha hema wake nafika nakhala pa mitengo yathundu ya pa Mamure, imene ili mu Hebroni, nammangira Yehova kumeneko guwa la nsembe.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 13:18

6

GENESIS 13:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Loti anatukula maso ake nayang'ana chigwa chonse cha Yordani kuti chonsecho chinali ndi madzi ambiri, asanaononge Yehova Sodomu ndi Gomora, monga munda wa Yehova, monga dziko la Ejipito pakunka ku Zowari.

Vergelijk

Ontdek GENESIS 13:10

Gratis leesplannen en overdenkingen die te maken hebben met GENESIS 13

Vorig hoofdstuk
Volgend hoofdstuk
YouVersion

Moedigt jou aan en daagt je uit om elke dag gemeenschap met God te zoeken.

Bediening

Over

Carrières

Vrijwilliger

Blog

Pers

Nuttige links

Help

Bijdragen

Bijbelvertalingen

Luisterbijbels

Bijbeltalen

Tekst van de Dag


Een digitale bediening van

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

PrivacybeleidVoorwaarden
Programma voor openbaarmaking van kwetsbaarheden
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Thuisscherm

Bijbel

Leesplannen

Video's