1
Gen. 7:1
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Chauta adauza Nowa kuti, “Loŵa m'chombo iwe pamodzi ndi banja lako. Iwe wekha ndakupeza kuti ndiwe wochita zondikondweretsa mu mbadwo uno.
နှိုင်းယှဉ်
Gen. 7:1ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
2
Gen. 7:24
Madziwo adakhala osaphwa konse pa dziko lapansi masiku 150.
Gen. 7:24ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
3
Gen. 7:11
Pa 17, mwezi wachiŵiri, Nowa ali wa zaka 600, akasupe onse a madzi ambiri okhala pansi pa dziko adatumphuka, ndipo kuthambo kudatsekukanso, kuti madzi akhuthuke.
Gen. 7:11ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
4
Gen. 7:23
Chauta adaononga zamoyo zonse za pa dziko: anthu, nyama, zokwaŵa ndi mbalame. Nowa yekha adapulumuka pamodzi ndi onse amene anali naye m'chombomo.
Gen. 7:23ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
5
Gen. 7:12
Choncho mvula idagwa pa dziko lapansi masiku makumi anai, usana ndi usiku.
Gen. 7:12ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
ပင်မစာမျက်နှာ
သမ္မာကျမ်းစာ
အစီအစဉ်များ
ဗီဒီယိုများ