1
Genesis 2:24
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
Nʼchifukwa chake, mwamuna amasiya abambo ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake ndipo awiriwo amakhala thupi limodzi.
နှိုင်းယှဉ်
Genesis 2:24ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
2
Genesis 2:18
Ndipo Yehova Mulungu anati, “Sibwino kuti munthu akhale yekha. Ndidzamupangira mnzake womuthandiza.”
Genesis 2:18ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
3
Genesis 2:7
Tsono Yehova Mulungu anawumba munthu kuchokera ku dothi nawuziramo mpweya wamoyo mʼmphuno mwake ndipo munthuyo anakhala wamoyo.
Genesis 2:7ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
4
Genesis 2:23
Munthu uja anati, “Uyu ndiye fupa lochokera ku mafupa anga ndi mnofu wochokera ku mnofu wanga; adzatchedwa ‘mkazi,’ popeza wachokera mwa mwamuna.”
Genesis 2:23ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
5
Genesis 2:3
Ndipo Mulungu anadalitsa tsiku lachisanu ndi chiwiri nalipatula, chifukwa pa tsiku limeneli Iye anapumula ku ntchito yonse yolenga imene anayigwira.
Genesis 2:3ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
6
Genesis 2:25
Munthu uja ndi mkazi wakeyo, onse awiri anali maliseche ndipo analibe manyazi.
Genesis 2:25ရှာဖွေလေ့လာလိုက်ပါ။
YouVersion သည် သင့်အတွေ့အကြုံကို စိတ်ကြိုက်ပြင်ဆင်ရန် ကွတ်ကီးများကို အသုံးပြုသည်။ ကျွန်ုပ်တို့၏ဝဘ်ဆိုဒ်ကိုအသုံးပြုခြင်းဖြင့် ကျွန်ုပ်တို့၏ ကိုယ်ရေးကိုယ်တာမူဝါဒတွင်ဖော်ပြထားသည့်အတိုင်း ကျွန်ုပ်တို့၏ cookies အသုံးပြုမှုကို သင်လက်ခံပါသည်။
ပင်မစာမျက်နှာ
ကျမ်းစာ
အစီအစဉ်
ဗီဒီယို