1
MARKO 3:35
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti aliyense achita chifuniro cha Mulungu, yemweyo ndiye mbale wanga, ndi mlongo, ndi amai.
ႏွိုင္းယွဥ္
MARKO 3:35ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
MARKO 3:28-29
Indetu, ndinena ndi inu, Adzakhululukidwa machimo onse a ana a anthu, ndi zamwano zilizonse adzachita mwano nazo; koma aliyense adzachitira Mzimu Woyera mwano alibe kukhululukidwa nthawi yonse, koma anapalamuladi tchimo losatha
MARKO 3:28-29ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
MARKO 3:24-25
Ndipo ufumu ukagawanika pa uwu wokha, sukhoza kukhazikika. Ndipo nyumba ikagawanika pa iyo yokha, sikhoza kukhazikika nyumbayo
MARKO 3:24-25ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
MARKO 3:11
Ndipo mizimu yonyansa, m'mene inamuona Iye, inamgwadira, nifuula, niti, Inu ndinu Mwana wa Mulungu.
MARKO 3:11ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား