1
MARKO 1:35
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo m'mawa mwake anauka usikusiku, natuluka namuka kuchipululu, napemphera kumeneko.
ႏွိုင္းယွဥ္
MARKO 1:35ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
MARKO 1:15
nanena, Nthawi yakwanira, ndipo Ufumu wa Mulungu wayandikira; tembenukani mtima, khulupirirani Uthenga Wabwino.
MARKO 1:15ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
MARKO 1:10-11
Ndipo pomwepo, alimkukwera potuluka m'madzi, anaona Iye thambo litang'ambika, ndi Mzimu alikutsikira pa Iye monga nkhunda: ndipo mau anatuluka m'thambo, Mwana wanga wokondedwa ndiwe, mwa Iwe ndikondwera bwino.
MARKO 1:10-11ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
4
MARKO 1:8
Ndakubatizani inu ndi madzi; koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera.
MARKO 1:8ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
5
MARKO 1:17-18
Ndipo Yesu ananena nao, Idzani pambuyo panga, ndipo ndidzakusandutsani inu asodzi a anthu. Ndipo pomwepo anasiya makoka ao, namtsata Iye.
MARKO 1:17-18ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
6
MARKO 1:22
Ndipo anazizwa ndi chiphunzitso chake; pakuti anaphunzitsa monga mwini mphamvu, si monga alembi.
MARKO 1:22ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား