1
LEVITIKO 11:45
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti Ine ndine Yehova amene ndinakukwezani kukutulutsani m'dziko la Ejipito, ndikhale Mulungu wanu; chifukwa chake mukhale oyera, popeza Ine ndine woyera.
ႏွိုင္းယွဥ္
LEVITIKO 11:45ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
LEVITIKO 11:44
Pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu; potero dzipatuleni, ndipo muzikhala oyera; pakuti Ine ndine woyera; ndipo musamadziipsa ndi chokwawa chilichonse chakukwawa pansi.
LEVITIKO 11:44ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား