1
LEVITIKO 10:1
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo ana a Aroni, Nadabu ndi Abihu anatenga yense mbale yake ya zofukiza, naikamo moto, naikapo chofukiza, nabwera nao pamaso pa Yehova moto wachilendo, umene sanawauze.
ႏွိုင္းယွဥ္
LEVITIKO 10:1ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
2
LEVITIKO 10:3
Ndipo Mose anati kwa Aroni, Ichi ndi chimene Yehova ananena, ndi kuti, Mwa iwo akundiyandikiza ndipatulidwa Ine, ndi pamaso pa anthu onse ndilemekezedwa. Ndipo Aroni anakhala chete.
LEVITIKO 10:3ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
3
LEVITIKO 10:2
Ndipo panatuluka moto pamaso pa Yehova, nuwatha, nafa iwo pamaso ya Yehova.
LEVITIKO 10:2ရွာေဖြေလ့လာလိုက္ပါ။
ပင္မစာမ်က္ႏွာ
သမၼာက်မ္းစာ
အစီအစဥ္မ်ား
ဗီဒီယိုမ်ား