YouVersion लोगो
सर्च आयकॉन

LUKA 14:13-14

LUKA 14:13-14 BLPB2014

Koma pamene ukonza phwando uitane aumphawi, opunduka, otsimphina, akhungu; ndipo udzakhala wodala; chifukwa iwo alibe chakubwezera iwe mphotho; pakuti idzabwezedwa mphotho pa kuuka kwa olungama.

LUKA 14 वाचा

ऐका LUKA 14

संबंधित व्हिडिओ