1
Maluko 9:23
Nyanja
NTNYBL2025
Yesu wadamkambila, “Ngati uli ni chikhulupililo, yonjhe yakhozeka kwa uyo wakhulupilila.”
താരതമ്യം
Maluko 9:23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
Maluko 9:24
Pampajha, tate wa yujha mwana wadalila kwa mvekelo, “Nikhulupilila! Nambho chikhulupililo changa chaching'ono, nithangatileni kuti nikhoze kukhulupilila.”
Maluko 9:24 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
Maluko 9:28-29
Ndiipo, Yesu yapo wadalowa mnyumba, oyaluzidwa wake adamfunjha paokha, “Ndande yanji ife sitidakhoze kumchocha chiwanda chijha?” Yesu wadaakambila, “Chiwanda ngati ichi sichikoza kuchoka, ingakhale kwa kupembhelape.”
Maluko 9:28-29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
Maluko 9:50
Mchele ni wabwino, nambho ngati ukataiza kukoma kwake, siuthilidwe chiyani kuti ukomenjho? Mkhale ngati mchele uwo ukoma, ni mkhale kwa mtendele ni achanjanu.”
Maluko 9:50 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
Maluko 9:37
“Mundhu waliyonjhe uyo wamlandila mwana wamng'ono ngati uyu ndande yaine wanilandila ine, ni siwanilandila inepe, chinchijha wamlandila Mnungu uyo wanituma.”
Maluko 9:37 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
Maluko 9:41
Zenedi nikukambilani, mundhu waliyonjhe uyo siwakupacheni chikho cha majhi ya kumwa, ndande ya anyiimwe ni wandhu wake Kilisito, mundhu mmeneyo siwalandile mbhaso yake.”
Maluko 9:41 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
7
Maluko 9:42
“Mundhu waliyonhje uyo siwamchitiche wana yawa anikhulupilila ine achite machimo, idakakhala bwino mundhu mmeneyo wamangwidwe mbhelo ya ikulu pakhosi ni kutaidwa mnyanja yamchele.
Maluko 9:42 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
8
Maluko 9:47
Ni diso lako likakuchiticha uchite machimo, lizule, mbasa kulowa mu umoyo wa muyaya uku uli ni diso limojhipe, kusiyana kukhala ni maso yonjhe yawili ni kutaidwa mumoto wa muyaya.
Maluko 9:47 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ