1
MARKO 7:21-23
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Pakuti m'kati mwake mwa mitima ya anthu, mutuluka maganizo oipa, zachiwerewere, zakuba, zakupha, zachigololo, masiriro, zoipa, chinyengo, chinyanso, diso loipa, mwano, kudzikuza, kupusa: zoipa izi zonse zituluka m'kati, nizidetsa munthu.
താരതമ്യം
MARKO 7:21-23 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MARKO 7:15
kulibe kanthu kunja kwa munthu kukalowa mwa iye, kangathe kumdetsa: koma zinthu zakutuluka mwa munthu, ndizo zakumdetsa munthu.
MARKO 7:15 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MARKO 7:6
Ndipo Iye ananena nao, Yesaya ananenera bwino za inu onyenga, monga mwalembedwa, Anthu awa andilemekeza Ine ndi milomo yao, koma mtima wao ukhala kutali ndi Ine.
MARKO 7:6 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MARKO 7:7
Koma andilambira Iye kwachabe, ndi kuphunzitsa maphunzitso, malangizo a anthu.
MARKO 7:7 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MARKO 7:8
Musiya lamulo la Mulungu, nimusunga mwambo wa anthu.
MARKO 7:8 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ