1
MATEYU 4:4
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma Iye anayankha nati, Kwalembedwa, Munthu sadzakhala ndi moyo ndi mkate wokha, koma ndi mau onse akutuluka m'kamwa mwa Mulungu.
താരതമ്യം
MATEYU 4:4 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 4:10
Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Choka Satana, pakuti kwalembedwa, Ambuye Mulungu wako udzamgwadira, ndipo Iye yekhayekha udzamlambira.
MATEYU 4:10 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 4:7
Yesu ananena naye, Ndiponso kwalembedwa, Usamuyese Ambuye Mulungu wako.
MATEYU 4:7 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 4:1-2
Pamenepo Yesu anatengedwa ndi Mzimu kunka kuchipululu kukayesedwa ndi mdierekezi. Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala.
MATEYU 4:1-2 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 4:19-20
Ndipo Iye ananena nao, Tiyeni pambuyo panga, ndidzakusandutsani asodzi a anthu. Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.
MATEYU 4:19-20 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MATEYU 4:17
Kuyambira pamenepo Yesu anayamba kulalikira, ndi kunena, Tembenukani mitima, pakuti Ufumu wa Kumwamba wayandikira.
MATEYU 4:17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ