1
MATEYU 3:8
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Onetsani inu zipatso zakuyenera kutembenuka mtima
താരതമ്യം
MATEYU 3:8 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
MATEYU 3:17
ndipo onani, mau akuchokera kumiyamba akuti, Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa, mwa Iyeyu ndikondwera.
MATEYU 3:17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
MATEYU 3:16
Ndipo Yesu, pamene anabatizidwa, pomwepo anatuluka m'madzi: ndipo onani, miyamba inamtsegukira Iye, ndipo anapenya Mzimu wa Mulungu wakutsika ngati nkhunda nudza nutera pa Iye
MATEYU 3:16 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
MATEYU 3:11
Inetu ndikubatizani inu ndi madzi kuloza ku kutembenuka mtima; koma Iye wakudza pambuyo panga, ali wakundiposa mphamvu, amene sindiyenera kunyamula nsapato zake: Iyeyu adzakubatizani inu ndi Mzimu Woyera ndi moto
MATEYU 3:11 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
MATEYU 3:10
Ndiponso tsopano lino nkhwangwa yaikidwa pa mizu ya mitengo: chifukwa chake mtengo uliwonse wosabala zipatso zabwino udulidwa nuponyedwa pamoto.
MATEYU 3:10 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
6
MATEYU 3:3
Pakuti uyu ndiye ananenayo Yesaya mneneri, kuti, Mau a wofuula m'chipululu, konzani khwalala la Ambuye, lungamitsani njira zake.
MATEYU 3:3 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ