1
GENESIS 19:26
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Koma mkazi wake anacheuka ali pambuyo pake pa Loti, nasanduka mwala wamchere.
താരതമ്യം
GENESIS 19:26 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
GENESIS 19:16
Koma anachedwa; ndipo anthuwo anamgwira dzanja lake, ndi dzanja la mkazi wake ndi dzanja la ana ake akazi awiri; chifukwa cha kumchitira chifundo Yehova; ndipo anamtulutsa iye, namuika kunja kwa mudzi.
GENESIS 19:16 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
GENESIS 19:17
Ndipo panali pamene anawatulutsa iwo kunja, anati, Tapulumuka ndi moyo wako; usacheuke, usakhale pachigwa paliponse; thawira kuphiri, kuti unganyeke.
GENESIS 19:17 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
GENESIS 19:29
Ndipo panali pamene Mulungu anaononga midzi ya m'chigwa, Mulungu anakumbukira Abrahamu, natulutsa Loti pakati pa chionongeko, pamene anaononga midzi m'mene anakhalamo Loti.
GENESIS 19:29 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ