1
GENESIS 18:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.
താരതമ്യം
GENESIS 18:14 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
2
GENESIS 18:12
ndipo Sara anaseka m'mtima mwake, nati, Kodi ndidzakhala ndi kukondwa ine nditakalamba, ndiponso mbuyanga ali wokalamba?
GENESIS 18:12 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
3
GENESIS 18:18
Pakuti Abrahamu adzakhala ndithu wamkulu ndi wamphamvu, ndipo mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsika mwa iye?
GENESIS 18:18 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
4
GENESIS 18:23-24
Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Kapena alipo olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi; kodi mudzaononga, simudzasiya malowo chifukwa cha olungama makumi asanu ali momwemo?
GENESIS 18:23-24 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
5
GENESIS 18:26
Ndipo anati Yehova, Ndikapeza m'Sodomu olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi, ndidzasiya malo onse chifukwa cha iwo.
GENESIS 18:26 പര്യവേക്ഷണം ചെയ്യുക
ആദ്യത്തെ സ്ക്രീൻ
വേദപുസ്തകം
പദ്ധതികൾ
വീഡിയോകൾ