Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from Gen. 2

1

Gen. 2:24

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Nchifukwa chake mwamuna amasiya atate ndi amai, ndipo amaphatikana ndi mkazi wake, choncho aŵiriwo amakhala thupi limodzi.

Bera saman

Njòttu Gen. 2:24

2

Gen. 2:18

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Pambuyo pake Chauta adati, “Sibwino kuti munthuyu akhale yekha. Ndipanga mnzake woti azimthandiza.”

Bera saman

Njòttu Gen. 2:18

3

Gen. 2:7

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Tsono Chauta adatenga dothi pa nthaka, ndipo adaumba munthu ndi dothilo. Adamuuzira mpweya wopatsa moyo m'mphuno zake, ndipo munthuyo adakhala wamoyo.

Bera saman

Njòttu Gen. 2:7

4

Gen. 2:23

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Adamu adati, “Uyutu ndiye ndi fupa lochokera ku mafupa anga, mnofu wochokera ku mnofu wanga. Adzatchedwa Mkazi, chifukwa watengedwa kwa Mwamuna.”

Bera saman

Njòttu Gen. 2:23

5

Gen. 2:3

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mulungu adadalitsa tsiku lachisanu ndi chiŵirilo, naliyeretsa, chifukwa choti pa tsiku limenelo adapuma atatsiriza zonse zimene ankachita.

Bera saman

Njòttu Gen. 2:3

6

Gen. 2:25

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

BLY-DC

Mwamunayo ndi mkazi wake uja, onse anali maliseche, komabe sankachita manyazi.

Bera saman

Njòttu Gen. 2:25

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast Gen. 2

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd