Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from YOHANE 9

1

YOHANE 9:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.

Bera saman

Njòttu YOHANE 9:4

2

YOHANE 9:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.

Bera saman

Njòttu YOHANE 9:5

3

YOHANE 9:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.

Bera saman

Njòttu YOHANE 9:2-3

4

YOHANE 9:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.

Bera saman

Njòttu YOHANE 9:39

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast YOHANE 9

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd