Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from GENESIS 7

1

GENESIS 7:1

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova kwa Nowa, Talowani, iwe ndi akunyumba ako onse m'chingalawamo; chifukwa ndakuona iwe kuti uli wolungama pamaso panga m'mbadwo uno.

Bera saman

Njòttu GENESIS 7:1

2

GENESIS 7:24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anapambana madzi pa dziko lapansi masiku zana kudza makumi asanu.

Bera saman

Njòttu GENESIS 7:24

3

GENESIS 7:11

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chaka cha mazana asanu ndi limodzi cha moyo wa Nowa, mwezi wachiwiri, tsiku la khumi ndi asanu ndi awiri la mwezi, tsiku lomwelo akasupe onse a madzi aakulu anasefuka, ndi mazenera a kumwamba anatseguka.

Bera saman

Njòttu GENESIS 7:11

4

GENESIS 7:23

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo zinaonongedwa zamoyo zonse zimene zinali pa dziko lapansi, anthu, ndi nyama, ndi zokwawa, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndipo zinaonongedwa pa dziko lapansi: anatsala Nowa yekha ndi amene anali pamodzi naye m'chingalawa.

Bera saman

Njòttu GENESIS 7:23

5

GENESIS 7:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo mvula inali pa dziko lapansi masiku makumi anai usana ndi usiku.

Bera saman

Njòttu GENESIS 7:12

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast GENESIS 7

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd