Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from GENESIS 41

1

GENESIS 41:16

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anayankha Farao kuti, Si mwa ine; koma Mulungu adzayankha Farao mwamtendere.

Bera saman

Njòttu GENESIS 41:16

2

GENESIS 41:38

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Farao anati kwa anyamata ake, Kodi ife tidzaone munthu ngati uyu, mzimu wa Mulungu uli m'mtima mwake?

Bera saman

Njòttu GENESIS 41:38

3

GENESIS 41:39-40

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Farao anati kwa Yosefe, Popeza Mulungu wakuonetsa iwe zonsezo palibe wina wakuzindikira ndi wanzeru ngati iwe. Uziyang'anira pa nyumba yanga, ndipo anthu anga onse adzalamulidwa mwa mau ako; pa mpando wachifumu pokha ine ndidzakuposa iwe.

Bera saman

Njòttu GENESIS 41:39-40

4

GENESIS 41:52

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo dzina la wachiwiri anamutcha Efuremu: chifukwa Mulungu anandibalitsa ine m'dziko la kusauka kwanga.

Bera saman

Njòttu GENESIS 41:52

5

GENESIS 41:51

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yosefe anamutcha dzina la woyamba Manase, chifukwa anati iye, Mulungu wandiiwalitsa ine zovuta zanga zonse, ndi nyumba yonse ya atate wanga.

Bera saman

Njòttu GENESIS 41:51

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast GENESIS 41

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd