Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from GENESIS 18

1

GENESIS 18:14

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.

Bera saman

Njòttu GENESIS 18:14

2

GENESIS 18:12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

ndipo Sara anaseka m'mtima mwake, nati, Kodi ndidzakhala ndi kukondwa ine nditakalamba, ndiponso mbuyanga ali wokalamba?

Bera saman

Njòttu GENESIS 18:12

3

GENESIS 18:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakuti Abrahamu adzakhala ndithu wamkulu ndi wamphamvu, ndipo mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsika mwa iye?

Bera saman

Njòttu GENESIS 18:18

4

GENESIS 18:23-24

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Kapena alipo olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi; kodi mudzaononga, simudzasiya malowo chifukwa cha olungama makumi asanu ali momwemo?

Bera saman

Njòttu GENESIS 18:23-24

5

GENESIS 18:26

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo anati Yehova, Ndikapeza m'Sodomu olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi, ndidzasiya malo onse chifukwa cha iwo.

Bera saman

Njòttu GENESIS 18:26

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast GENESIS 18

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd