1
GENESIS 18:14
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.
Bera saman
Njòttu GENESIS 18:14
2
GENESIS 18:12
ndipo Sara anaseka m'mtima mwake, nati, Kodi ndidzakhala ndi kukondwa ine nditakalamba, ndiponso mbuyanga ali wokalamba?
Njòttu GENESIS 18:12
3
GENESIS 18:18
Pakuti Abrahamu adzakhala ndithu wamkulu ndi wamphamvu, ndipo mitundu yonse ya dziko lapansi idzadalitsika mwa iye?
Njòttu GENESIS 18:18
4
GENESIS 18:23-24
Ndipo Abrahamu anayandikira nati, Kodi mudzaononga olungama pamodzi ndi oipa? Kapena alipo olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi; kodi mudzaononga, simudzasiya malowo chifukwa cha olungama makumi asanu ali momwemo?
Njòttu GENESIS 18:23-24
5
GENESIS 18:26
Ndipo anati Yehova, Ndikapeza m'Sodomu olungama makumi asanu m'kati mwa mudzi, ndidzasiya malo onse chifukwa cha iwo.
Njòttu GENESIS 18:26
Heim
Biblía
Áætlanir
Myndbönd