Merki YouVersion
BiblíaÁætlanirMyndbönd
Sæktu forritið
Language Selector
Search Icon

Popular Bible Verses from LUKA 19

1

LUKA 19:10

Buku Lopatulika

BLP-2018

Pakuti Mwana wa Munthu anadza kufunafuna ndi kupulumutsa chotayikacho.

Bera saman

Njòttu LUKA 19:10

2

LUKA 19:38

Buku Lopatulika

BLP-2018

nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere mu Mwamba, ndi ulemerero mu Mwambamwamba.

Bera saman

Njòttu LUKA 19:38

3

LUKA 19:9

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Yesu anati kwa iye, Lero chipulumutso chagwera nyumba iyi, popeza iyenso ndiye mwana wa Abrahamu.

Bera saman

Njòttu LUKA 19:9

4

LUKA 19:5-6

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo m'mene anadza pamalopo Yesu anakweza maso nati kwa iye, Zakeyo, fulumira, nutsike; pakuti lero ndiyenera kukhala m'nyumba mwako. Ndipo anafulumira, natsika, namlandira Iye wokondwera.

Bera saman

Njòttu LUKA 19:5-6

5

LUKA 19:8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Zakeyo anaimirira nati kwa Ambuye, Taonani, Ambuye, gawo limodzi la zanga zonse zogawika pakati ndipatsa osauka; ndipo ngati ndalanda kanthu kwa munthu monyenga, ndimbwezera kanai.

Bera saman

Njòttu LUKA 19:8

6

LUKA 19:39-40

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

Bera saman

Njòttu LUKA 19:39-40

Ókeypis lestraráætlanir og hugleiðingar sem tengjast LUKA 19

Fyrri kafli
Næsti kafli
YouVersion

Hvetur þig áfram og skorar á þig að leita samfélags við Guð á hverjum degi.

Kirkjustarf

Um YouVersion

Starfsferill

Sjálfboðaliði

Blogg

Fjölmiðlar

Gagnlegar hlekkir

Hjálp

Gefa

Bíblíuútgáfa

Hljóðbiblíur

Tungumál Biblíunnar

Vers dagsins


Stafræn kirkja

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

FriðhelgisstefnaSkilmálar
Vulnerability Disclosure Program
FacebookTwitterInstagramYoutubePinterest

Heim

Biblía

Áætlanir

Myndbönd