1
MARKO 15:34
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine?
Konpare
Eksplore MARKO 15:34
2
MARKO 15:39
Ndipo pamene kenturiyo, woimirirapo popenyana ndi Iye, anaona kuti anapereka mzimu kotero, anati, Zoonadi, munthu uyu anali Mwana wa Mulungu.
Eksplore MARKO 15:39
3
MARKO 15:38
Ndipo chinsalu chotchinga cha m'Kachisi chinang'ambika pakati, kuyambira kumwamba kufikira pansi.
Eksplore MARKO 15:38
4
MARKO 15:37
Ndipo Yesu anatulutsa mau okweza, napereka mzimu wake.
Eksplore MARKO 15:37
5
MARKO 15:33
Ndipo pofika ora lachisanu ndi chimodzi, panali mdima pa dziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.
Eksplore MARKO 15:33
6
MARKO 15:15
Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.
Eksplore MARKO 15:15
Akèy
Bib
Plan yo
Videyo