Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan MARKO 15

1

MARKO 15:34

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pa ora lachisanu ndi chinai Yesu anafuula ndi mau okweza, Eloi, Eloi, lama sabakitani? ndiko kusandulika, Mulungu wanga, Mulungu wanga mwandisiyiranji Ine?

Konpare

Eksplore MARKO 15:34

2

MARKO 15:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pamene kenturiyo, woimirirapo popenyana ndi Iye, anaona kuti anapereka mzimu kotero, anati, Zoonadi, munthu uyu anali Mwana wa Mulungu.

Konpare

Eksplore MARKO 15:39

3

MARKO 15:38

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo chinsalu chotchinga cha m'Kachisi chinang'ambika pakati, kuyambira kumwamba kufikira pansi.

Konpare

Eksplore MARKO 15:38

4

MARKO 15:37

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anatulutsa mau okweza, napereka mzimu wake.

Konpare

Eksplore MARKO 15:37

5

MARKO 15:33

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo pofika ora lachisanu ndi chimodzi, panali mdima pa dziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.

Konpare

Eksplore MARKO 15:33

6

MARKO 15:15

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.

Konpare

Eksplore MARKO 15:15

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak MARKO 15

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo