Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan LUKA 16

1

LUKA 16:10

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Iye amene akhulupirika m'chaching'onong'ono alinso wokhulupirika m'chachikulu; ndipo iye amene ali wosalungama m'chachikulu.

Konpare

Eksplore LUKA 16:10

2

LUKA 16:13

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Palibe mnyamata wa m'nyumba akhoza kukhala kapolo wa ambuye awiri; pakuti kapena adzamuda wina, nadzakonda winayo; kapena adzatsata wina, nadzapeputsa winayo. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Chuma.

Konpare

Eksplore LUKA 16:13

3

LUKA 16:11-12

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Chifukwa chake ngati simunakhala okhulupirika m'chuma cha chosalungama, adzakhulupirira inu ndani ndi chuma choona? Ndipo ngati simunakhala okhulupirika ndi zake za wina, adzakupatsani inu ndani za inu eni?

Konpare

Eksplore LUKA 16:11-12

4

LUKA 16:31

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Koma anati kwa iye, Ngati samvera Mose ndi aneneri, sadzakopeka mtima ngakhale wina akauka kwa akufa.

Konpare

Eksplore LUKA 16:31

5

LUKA 16:18

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Yense wakusudzula mkazi wake, nakwatira wina, achita chigololo; ndipo iye amene akwatira wosudzulidwayo, achita chigololo.

Konpare

Eksplore LUKA 16:18

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak LUKA 16

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo