Logo YouVersion
BibPlan yoVideyo
Pran aplikasyon an
Seleksyone Lang
Chache Icon

Vèsè popilè nan Bib la ki soti nan YOHANE 9

1

YOHANE 9:4

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Tiyenera kugwira ntchito za Iye wondituma Ine, pokhala pali msana; ukudza usiku pamene palibe munthu angakhoze kugwira ntchito.

Konpare

Eksplore YOHANE 9:4

2

YOHANE 9:5

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Pakukhala Ine m'dziko lapansi, ndili kuunika kwa dziko lapansi.

Konpare

Eksplore YOHANE 9:5

3

YOHANE 9:2-3

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo ophunzira ake anamfunsa Iye, nanena, Rabi, anachimwa ndani, ameneyo, kapena atate wake ndi amake, kuti anabadwa wosaona? Yesu anayankha, Sanachimwe ameneyo, kapena atate wake ndi amake; koma kuti ntchito za Mulungu zikaonetsedwe mwa iye.

Konpare

Eksplore YOHANE 9:2-3

4

YOHANE 9:39

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

BLPB2014

Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.

Konpare

Eksplore YOHANE 9:39

Plan lekti ak devosyon gratis yo ki gen rapò ak YOHANE 9

Chapit Avan yo
Chapit suivan
YouVersion

Ankouraje ak defi pou w chèche entimite ak Bondye chak jou.

Ministè

Apwopo

Karyè yo

Volontè

Blòg

Peze

Lyen itil yo

Ed

Fè yon don

Vèsyon Bib yo

Odyo Bib yo

Diferan Lang yo nan Bib la

Vèsè Jodi a


Yon Ministè Digital nan

Life.Church
English (US)

©2025 Life.Church / YouVersion

Politik PriveTèm yo
Pwogram Divilgasyon Vilnerabilite
FacebookTwitterInstagramYouTubePinterest

Akèy

Bib

Plan yo

Videyo